Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 November tsamba 5
  • Nsembe Yosonyeza Kuyamikira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nsembe Yosonyeza Kuyamikira
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • “Dzisonyezeni Inueni Kukhala Akuyamika”
    Nsanja ya Olonda—1988
  • Sonyezani Kuyamikira Kwanu
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2004
  • Tizisonyeza Kuti Ndife Oyamikira
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Zimene Tingaphunzire M’buku la Levitiko
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 November tsamba 5
Banja la Chiisiraeli likudya nyama yoperekedwa monga nsembe yachiyanjano.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | LEVITIKO 6-7

Nsembe Yosonyeza Kuyamikira

7:11-15, 20

Nsembe zachiyanjano zimene Aisiraeli ankapereka zimatikumbutsa kufunika koyamikira Yehova kudzera m’mapemphero komanso m’makhalidwe athu.​—Afi 4:6, 7; Akl 3:15.

  • Tikamapemphera, kodi tingathokoze Yehova chifukwa cha zinthu ziti?​—1At 5:17, 18

  • Kodi kusonyeza kuti ndife oyamikira kumatithandiza bwanji?

  • Kodi munthu angamadye bwanji “patebulo la ziwanda,” nanga zimenezi zingasonyeze bwanji kuti munthuyo sayamikira Yehova?​—1Ak 10:20, 21

Mkazi wa Chiisiraeli akuyang’ana kumwamba ndipo akuthokoza Yehova.
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena