Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 January tsamba 16
  • Zimene Tinganene

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tinganene
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Ulendo Woyamba
  • Ulendo Wobwereza
  • Ntchito Yoitanira Anthu ku Chikumbutso (27 February–27 March)
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 January tsamba 16

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

Zimene Tinganene

Ulendo Woyamba

Funso: Kodi Mulungu amamvetsera mapemphero athu?

Lemba: Sl 65:2

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi ndi zinthu ziti zomwe tingatchule m’mapemphero athu?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • ‘Nsanja ya Olonda’ Na. 1 2021.

    wp21.1 5

Ulendo Wobwereza

Funso: Kodi ndi zinthu ziti zomwe tingatchule m’mapemphero athu?

Lemba: 1Yo 5:14

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi Mulungu amayankha bwanji mapemphero athu?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • ‘Nsanja ya Olonda’ Na. 1 2021.

    wp21.1 10

Ntchito Yoitanira Anthu ku Chikumbutso (27 February–27 March)

“Tabwera [kapena takuimbirani kapenanso takulemberani] kuti tikuitanireni kumwambo wofunika kwambiri womwe udzachitike padziko lonse. Mwambo umenewu ndi wokumbukira imfa ya Yesu.” Kenako m’patseni kapepala [kapena mutumizireni meseji kapenanso imelo]. “Kapepalaka kakusonyeza nthawi komanso malo omwe mwambowu udzachitikire m’dera lathu lino [kapena zimene mungachite kuti muchite nawo mwambowu pa intaneti]. Tikukuitananinso kuti mudzamvetsere nkhani yapadera yomwe idzakambidwe kumapeto a mlungu woyambira March 15.”

Funso la Ulendo Wotsatira Ngati Munthuyo Wasonyeza Chidwi: N’chifukwa chiyani Yesu anafa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena