Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 April tsamba 1
  • Zimene Tinganene

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tinganene
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • ●○○ ULENDO WOYAMBA
  • ○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA
  • ○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI
  • NTCHITO YOITANIRA ANTHU KU CHIKUMBUTSO (March 14–April 7):
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 April tsamba 1
Yesu ndi atumwi ake akuchita mwambo wa Chakudya cha Madzulo cha Ambuye.

Yesu akuchita pangano ndi atumwi ake okhulupirika

Zimene Tinganene

●○○ ULENDO WOYAMBA

Funso: Kodi cholinga cha Mulungu polenga anthu chinali chotani?

Lemba: Ge 1:28

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi timadziwa bwanji kuti cholinga chomwe Mulungu analengera anthu chidzakwaniritsidwa?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • Buku lakuti ‘Zimene Baibulo Limaphunzitsa.’

    bhs 29 ¶1

○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA

Funso: Kodi timadziwa bwanji kuti cholinga chomwe Mulungu analengera anthu chidzakwaniritsidwa?

Lemba: Yes 55:11

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi moyo udzakhala wotani Mulungu akadzakwaniritsa cholinga chimene analengera anthu?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • Buku lakuti ‘Zimene Baibulo Limaphunzitsa.’

    bhs 29 ¶2

○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI

Funso: Kodi moyo udzakhala wotani Mulungu akadzakwaniritsa cholinga chomwe analengera anthu?

Lemba: Sl 37:10, 11

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi tingatani kuti tidzalandire madalitso amene Mulungu analonjeza?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • Buku lakuti ‘Zimene Baibulo Limaphunzitsa.’

    bhs 35 ¶17

NTCHITO YOITANIRA ANTHU KU CHIKUMBUTSO (March 14–April 7):

“Tikukuitanirani ku mwambo wofunika kwambiri womwe udzachitike padziko lonse. Mwambo umenewu ndi wokumbukira imfa ya Yesu.” Kenako m’patseni kapepala. “Kapepalaka kakusonyeza nthawi komanso malo omwe mwambowu udzachitikire m’dera lathu lino. Tikukuitananinso kuti mudzamvetsere nkhani yapadera yomwe idzakambidwe ­kumapeto a mlungu wa March 30.”

Funso la Ulendo Wotsatira Ngati Munthuyo Wasonyeza Chidwi: N’chifukwa chiyani Yesu anafa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena