Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 March tsamba 16
  • Zimene Tinganene

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tinganene
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Ntchito Yoitanira Anthu ku Chikumbutso (27 February–27 March)
  • Ulendo Woyamba
  • Ulendo Wobwereza
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 March tsamba 16

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

Zimene Tinganene

Ntchito Yoitanira Anthu ku Chikumbutso (27 February–27 March)

Kapepala koitanira anthu kumwambo wokumbukira imfa ya Yesu kamutu wakuti, ‘Ndinu Olandiridwa’

“Tabwera [kapena takuimbirani kapenanso takulemberani] kuti tikuitanireni kumwambo wofunika kwambiri womwe udzachitike padziko lonse. Mwambo umenewu ndi wokumbukira imfa ya Yesu.” Kenako m’patseni kapepala [kapena mutumizireni meseji kapenanso imelo]. “Kapepalaka kakusonyeza nthawi komanso malo omwe mwambowu udzachitikire m’dera lathu lino [kapena zimene mungachite kuti muchite nawo mwambowu pa intaneti]. Tikukuitananinso kuti mudzamvetsere nkhani yapadera yomwe idzakambidwe kumapeto a mlungu woyambira March 15.”

Ngati Munthuyo Wasonyeza Chidwi: Musonyezeni [kapena mutumizireni linki ya] vidiyo yakuti Tizikumbukira Imfa ya Yesu.

Funso la Ulendo Wotsatira: N’chifukwa chiyani Yesu anafa?

Ulendo Woyamba

Funso: Kodi Yesu anali ndani?

Lemba: Mt 16:16

Funso la Ulendo Wotsatira: N’chifukwa chiyani Yesu anafa?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • Buku lakuti ‘Zimene Baibulo Limaphunzitsa’

    bhs 41 ¶5

Ulendo Wobwereza

Funso: N’chifukwa chiyani Yesu anafa?

Lemba: Mt 20:28

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi tingasonyeze bwanji kuti timayamikira nsembe ya dipo ya Yesu?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • Buku lakuti ‘Zimene Baibulo Limaphunzitsa’

    bhs 52 ¶2

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena