Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 May tsamba 15
  • “Kodi Yehova Mulungu Wanu Akufuna Kuti Muzichita Chiyani?”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Kodi Yehova Mulungu Wanu Akufuna Kuti Muzichita Chiyani?”
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Kutumikira Yehova Sikovuta Kwambiri
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Baibulo Ndi Buku Limene Limanena Zoona
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Zimene Tingaphunzire pa Mafanizo a mu Nyimbo Youziridwa
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Kodi Muli ndi Mbiri Ngati ya Yobu?
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 May tsamba 15

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

“Kodi Yehova Mulungu Wanu Akufuna Kuti Muzichita Chiyani?”

Tizimvera Yehova chifukwa chomulemekeza kwambiri komanso kumukonda (De 10:12; w09 10/1 10 ¶3-4)

Kumvera kumabweretsa madalitso (De 10:13; w09 10/1 10 ¶6)

Yehova amafuna kuti tikhale naye paubwenzi wolimba (De 10:15; cl 16 ¶2)

Yehova satikakamiza kuti tizimumvera. M’malomwake, iye amafuna kuti tizimukonda komanso kumumvera “mochokera pansi pa mtima.” (Aro 6:17) Anthu amene asankha kutumikira Yehova amakhala moyo wosangalala kwambiri.

Mzimayi akusankha kutumikira Yehova. 1. Akumwa mowa komanso akusuta fodya. 2. Wakhudzidwa kwambiri ndi zimene akuphunzira pa phunziro la Baibulo. 3. Akucheza mosangalala ndi anzake amene amatumikira nawo Yehova.
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena