Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 March tsamba 3
  • Kumvera Kumaposa Nsembe

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kumvera Kumaposa Nsembe
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Kudzikuza Kumabweretsa Manyazi
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Muzimuuza Yehova Zamumtima Mwanu Mukamapemphera
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Kodi Mfumu Yanu ndi Ndani?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Mmene Davide Ankamenyera Nkhondo
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 March tsamba 3
Mfumu Sauli akuuza msilikali wa Chiisiraeli amene wanyamula lupanga kuti asaphe Agagi. Chakumbuyo kwawo kuli msilikali amene akukusa nkhosa.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kumvera Kumaposa Nsembe

Mneneri wa Yehova anapereka malangizo omveka bwino kwa Mfumu Sauli (1Sa 15:3)

Sauli anapereka zifukwa zodzikhululukira chifukwa sanamvere zonse zimene Yehova anamuuza (1Sa 15:13-15)

Yehova savomereza kulambira kwa anthu omwe samumvera (1Sa 15:22, 23; w07 6/15 26 ¶4; it-2 521 ¶2)

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndimamvera malangizo ochokera ku gulu la Yehova mwamsanga komanso ndi mtima wonse?’

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena