Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 September tsamba 8
  • Kodi Mumachita Zinthu Molimba Mtima Ngati Asa?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mumachita Zinthu Molimba Mtima Ngati Asa?
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • “Mudzapeza Mphoto Chifukwa cha Ntchito Yanu”
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Muzichita Zinthu Mwanzeru pa Nthawi Yomwe Zinthu Zikuyenda Bwino
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
  • Tizitumikira Yehova ndi Mtima Wathunthu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Zimene Yehova Wachita Kuti Tiyandikane Naye
    Nsanja ya Olonda—2014
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 September tsamba 8

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kodi Mumachita Zinthu Molimba Mtima Ngati Asa?

Asa anadzipereka poteteza kulambira koona (1Mf 15:11, 12; w12 8/15 8 ¶4)

Molimba mtima, Asa anasonyeza kuti kulambira Yehova kunali kofunika kwambiri kuposa anthu a m’banja lake (1Mf 15:13; w17.03 19 ¶7)

Ngakhale kuti Asa ankalakwitsa zinthu zina, Yehova ankamuonabe kuti anali wokhulupirika chifukwa cha makhalidwe ake abwino (1Mf 15:14, 23; it-1 184-185)

Mnyamata wanyamula sutikesi ndipo akuchoka pakhomo. Bambo wakumbatira mkazi ndi mwana wake omwe akulira.

DZIFUNSENI KUTI: ‘Kodi ndimasonyeza kuti ndimakonda kwambiri kulambira koona? Kodi ndimasiya kuchita zinthu ndi wina aliyense, ngakhale wachibale wanga, amene wasiya kutumikira Yehova?’​—2Yo 9, 10.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena