Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 September tsamba 9
  • Samalani ndi Nkhani Zabodza

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Samalani ndi Nkhani Zabodza
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Musamatsanzire Elifazi Potonthoza Ena
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Pewani Maganizo Olakwika
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Yobu Anapirira—Nafenso Tingatero!
    Nsanja ya Olonda—1994
  • Yobu Afupidwa Chifukwa Chokhulupirika
    Nsanja ya Olonda—1998
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 September tsamba 9

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Samalani ndi Nkhani Zabodza

Zimene Elifazi ankanena zinkaoneka ngati zoona chifukwa anali wamkulu komanso wanzeru (Yob 4:1; it-1 713 ¶11)

Ziwanda zinamutsogolera kuti akapereke uthenga wofooketsa kwa Yobu (Yob 4:​14-16; w05 9/15 26 ¶2)

Zina mwa zomwe Elifazi ananena zinali zoona, koma anazigwiritsa ntchito molakwika (Yob 4:19; w10 2/15 19 ¶5-6)

M’bale akuyang’ana pafoni yake.

Dziko la Satanali limafalitsa nkhani zabodza zowononga.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndimapeza nthawi yoti nditsimikizire kaye ngati nkhani zimene ndikumva kapena kuwerenga zilidi zoona?’—mrt 32 ¶13-17

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena