Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsamba 10
  • Sitifunika Kukhala Angwiro Kuti Tikhale Okhulupirika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Sitifunika Kukhala Angwiro Kuti Tikhale Okhulupirika
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Pitirizani Kukhala ndi Mtima Wosagawanika
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Tidzayenda Mogwirizana Ndi Mtima Wathu Wosagawanika
    Nsanja ya Olonda—2010
  • N’chifukwa Chiyani Muyenera Kusunga Umphumphu?
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Pitirizani Kusonyeza Kuti Mumakonda Kwambiri Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 November tsamba 10

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Sitifunika Kukhala Angwiro Kuti Tikhale Okhulupirika

Yobu analakwitsa podzudzula Mulungu (Yob 27:​1, 2)

Yobu ankadziona kuti ndi wokhulupirika ngakhale kuti ankalakwitsa zinthu zina (Yob 27:5; it-1 1210 ¶4)

Sitifunika kukhala angwiro kuti tikhale okhulupirika, chomwe chimangofunika ndi kukonda Yehova ndi mtima wonse (Mt 22:37; w19.02 3 ¶3-5)

M’bale akudziimba mlandu chifukwa cha zinthu zimene analakwitsa m’mbuyo. Kenako akuoneka osangalala ndipo sakudzikayikira.

FUNSO LOFUNIKA KULIGANIZIRA: Kodi Kudziwa kuti Yehova safuna kuti tizichita zinthu ngati anthu angwiro kumatithandiza bwanji kuti tisafooke?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena