Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w25 April tsamba 32
  • Zithunzi Zingakuthandizeni

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zithunzi Zingakuthandizeni
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2025
  • Nkhani Yofanana
  • “Zithunzi Zokongola Kwambiri”
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Kalata Yochokera ku Bungwe Lolamulira
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Kugwiritsa Ntchito Bwino Zinthu Zooneka
    Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso
  • Kuchokera kwa Owerenga
    Galamukani!—2006
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2025
w25 April tsamba 32

MFUNDO ZOTHANDIZA POPHUNZIRA

Zithunzi Zingakuthandizeni

Mabuku athu amakhala ndi zithunzi zomwe zingakuthandizeni kudziwa mfundo zofunika. Kodi mungatani kuti zithunzi zimenezi zizikuthandizani?

  • Muziona zithunzi musanawerenge nkhani yake. Zithunzi zimachititsa chidwi ndipo zingakulimbikitseni kuti muwerenge nkhaniyo. Zimakhala ngati “mwalawa” zimene mukufuna kuwerengazo. Choncho muzidzifunsa kuti, ‘Kodi ndikuona chiyani?’​—Amosi 7:7, 8.

  • Mukamawerenga nkhani muzidzifunsa chifukwa chake aikamo chithunzi. Muziwerenga mawu ofotokozera chithunzi ngati alipo. Muziona kugwirizana pakati pa chithunzicho ndi nkhaniyo komanso mmene mungagwiritsire ntchito zimene mukuphunzira.

  • Mukamaliza kuwerenga, muzionanso zithunzizo kuti mukumbukire mfundo zazikulu. Muziyesa kuonanso chithunzicho m’maganizo mwanu komanso mfundo imene munaphunzirapo.

  • Tayesani kuonanso zithunzi za m’magazini ino n’kuona ngati mukukumbukira zimene munaphunzira.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena