Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w25 August tsamba 32
  • Malifalensi a Malemba Angakuthandizeni

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Malifalensi a Malemba Angakuthandizeni
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2025
  • Nkhani Yofanana
  • Mungaphunzirenso Izi
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Mungaphunzirenso Izi
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Laibulale Yokwanira M’dzanja Limodzi
    Kodi Zopereka Zanu Zimagwiritsidwa Ntchito Bwanji?
  • Mungapeze Nzeru Zokuthandizani pa JW.ORG
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2025
w25 August tsamba 32

MFUNDO ZOTHANDIZA POPHUNZIRA

Malifalensi a Malemba Angakuthandizeni

Malifalensi a m’Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika amasonyeza kuti mbali zosiyanasiyana za Baibulo ndi zogwirizana, pokuthandizani kupeza malemba ena omwe ali ndi mfundo zowonjezereka pa nkhani imene mukuwerenga. Malifalensiwa ndi tizilembo ting’onoting’ono tomwe timapezeka kutsogolo kwa liwu. Mu Baibulo losindikizidwa mungapeze tizilembo tofanana nato mudanga lapakati kuti mupeze malemba ena omwe ali ndi nkhani yofanana nayo. Pa jw.org kapena pa JW Library® dinani kachilemboko kuti muone malemba ena.

Malifalensi angakuthandizeni kupeza zinthu monga:

Nkhani Yofanana Nayo: Lifalensi ingakutengereni ku malemba ena omwe ali ndi nkhani ina yofanana ndi nkhani yomwe mukuwerengayo. Mwachitsanzo, onani lemba la 2 Samueli 24:1 ndi 1 Mbiri 21:1.

Komwe Mawu Enaake Achokera: Lifalensi ingakuthandizeni kudziwa kumene mawu ena atengedwa. Mwachitsanzo, onani lemba la Mateyu 4:4 ndi Deuteronomo 8:3.

Kukwaniritsidwa kwa Ulosi: Lifalensi ingakuthandizeni kudziwa mmene ulosi winawake unakwaniritsidwira. Mwachitsanzo, onani lemba la Mateyu 21:5 ndi Zekariya 9:9.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena