Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yb16 tsamba 8-tsamba 9 ndime 1
  • Zimene Zachitika M’chaka Chapitachi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Zachitika M’chaka Chapitachi
  • Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2016
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mutsanzira Kudzipereka kwa Yehova ndi Yesu pa Nyengo ya Chikumbutso Ikubwerayi?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • “Yakani ndi Mzimu”
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Tiyeni Tipitirize Kukhala Achangu Muutumiki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2007
  • Khalani Odzipereka pa Kulambira Koona
    Nsanja ya Olonda—2010
Onani Zambiri
Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2016
yb16 tsamba 8-tsamba 9 ndime 1
A Mboni za Yehova akumanga ofesi ya omasulira m’chinenero cha Chiayimara ku El Alto m’dziko la Bolivia

Bolivia: Abale akumanga ofesi ya omasulira m’chinenero cha Chiayimara ku El Alto

Zimene Zachitika M’chaka Chapitachi

BAIBULO limasonyeza kuti Mulungu adzachita zinthu zosiyanasiyana pogwiritsa ntchito Ufumu wake. Ndipo lemba la Yesaya 9:7 limati, “Yehova wa makamu adzachita zimenezi modzipereka kwambiri.” Nayenso Yesu Khristu, yemwe ndi Mfumu ya Ufumuwu, anagwira ntchito modzipereka kwambiri pamene ankachita utumiki wake padziko lapansi. (Yoh. 2:17) Malipoti ali m’munsiwa akusonyeza kuti nawonso a Mboni za Yehova padziko lonse akutengera chitsanzo cha Yehova komanso Yesu. Iwo akuthandiza anthu kuona chikondi chimene Atate wathu Yehova, amatisonyeza.

Anthu akumvetsera nkhani pamsonkhano wachigawo wa 2015 wa Mboni za Yehova ku El Salvador

El salvador: Msonkhano wachigawo wa 2015

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena