Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Yonatani mwana wa Sauli+ anali ndi mwana wamwamuna wolumala mapazi.+ Mwanayu anali ndi zaka 5 pamene kunabwera uthenga wochokera ku Yezereeli+ wakuti Sauli ndi Yonatani afa. Uthengawu utafika, mayi amene ankamusamalira anamunyamula nʼkuyamba kuthawa. Pamene ankathawa mwamantha, mayiyo anagwetsa mwanayo ndipo analumala. Mwanayo dzina lake linali Mefiboseti.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena