Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 22:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma Yehosabati mwana wamkazi wa mfumu, anaba Yehoasi+ mwana wamwamuna wa Ahaziya, pagulu la ana aamuna a mfumu amene ankayenera kuphedwa. Anatenga Yehoasi ndi mayi amene ankamusamalira nʼkukamubisa mʼchipinda chamkati chogona. Yehosabati, mwana wamkazi wa Mfumu Yehoramu,+ (ameneyu anali mkazi wa wansembe Yehoyada+ komanso mchemwali wake wa Ahaziya) anakwanitsa kubisa mwanayo kuti Ataliya asamuone, moti sanaphedwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena