Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 34:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Choncho Yehova wanena kuti, ‘Inu simunamvere mawu anga oti mulengeze ufulu, aliyense kwa mʼbale wake ndi kwa mnzake.+ Tsopano ine ndikulengeza ufulu kwa inu,’ akutero Yehova. ‘Inu mudzafa ndi lupanga, mliri* ndi njala.+ Ndidzakusandutsani chinthu chimene maufumu onse apadziko lapansi adzachita nacho mantha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena