Levitiko 17:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 “‘Munthu aliyense wa nyumba ya Isiraeli kapena mlendo wokhala pakati panu, akadya magazi alionse,+ ndidzam’kana*+ ndipo ndidzamupha kuti asakhalenso pakati pa anthu amtundu wake. Levitiko Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 17:10 Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 39 Nsanja ya Olonda,11/15/2014, ptsa. 10-116/15/1991, tsa. 9
10 “‘Munthu aliyense wa nyumba ya Isiraeli kapena mlendo wokhala pakati panu, akadya magazi alionse,+ ndidzam’kana*+ ndipo ndidzamupha kuti asakhalenso pakati pa anthu amtundu wake.
17:10 Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 39 Nsanja ya Olonda,11/15/2014, ptsa. 10-116/15/1991, tsa. 9