15 Munthu uja anayezanso m’litali mwa nyumba ya kumadzulo ija imene inayang’anizana ndi mpata waukulu. Anayeza timakonde take mbali iyi ndi mbali inayo n’kupeza kuti nyumbayo ndi timakondeto zinali mikono 100.
Anayezanso kachisi, malo ake amkati+ ndi makonde oyang’ana kubwalo.