Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mika 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Otsala a Yakobo adzakhala pakati pa mitundu yambiri ya anthu. Iwo adzakhala ngati mkango pakati pa nyama zakutchire. Adzakhala ngati mkango wamphamvu pakati pa magulu ankhosa, umene umati ukadutsa pakati pa nkhosazo, ndithu umazimbwandira ndi kuzikhadzula+ ndipo sipakhala wozipulumutsa.

  • Mika
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 5:8

      Tsiku la Yehova, ptsa. 169-170

      Nsanja ya Olonda,

      11/1/2001, tsa. 11

      8/15/1990, ptsa. 30-31

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena