Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 May tsamba 3
  • Utumiki Wothandiza Anthu pa Nthawi ya Mavuto

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Utumiki Wothandiza Anthu pa Nthawi ya Mavuto
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Utumiki Wothandiza Anthu pa Nthawi ya Mavuto
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulira
  • Kodi Mudzachita Upainiya Wothandiza M’mwezi wa March Kapena April?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 May tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 2 AKORINTO 7-10

Utumiki Wothandiza Anthu pa Nthawi ya Mavuto

8:1-4; 9:7

Akhristufe tili ndi utumiki wa mbali ziwiri. Tili ndi “utumiki wokhazikitsanso mtendere” womwe timauchita tikamalalikira komanso kuphunzitsa anthu. Komanso tili ndi ‘utumiki wothandiza anthu’ womwe timachitira Akhristu anzathu. (2 Akor. 5:18-20; 8:4) Choncho tikamathandiza Akhristu anzathu omwe ali pamavuto, timakhala tikuchita utumiki wopatulika. Tikamagwira nawo ntchitoyi:

  • timathandiza abale ndi alongo athu kupeza zinthu zomwe akusowa.​—2 Akor. 9:12a

  • timathandiza anzathu omwe apanikizika ndi mavuto kuti ayambirenso kuchita zinthu zofunika potumikira Mulungu ndipo amayamba kulalikira mwakhama posonyeza kuyamikira kwawo Yehova.​—2 Akor. 9:12b

  • timathandiza kuti anthu alemekeze Yehova. (2 Akor. 9:13) Ntchito yothandiza anthu pa nthawi yangozi imakhala ngati njira yolalikirira anthu onse, ngakhalenso omwe amadana ndi Mboni za Yehova

Banja la m’nthawi yakale likupereka zopereka zawo; mlongo akuonerera pamene abale a m’komiti yopereka chithandizo akumukonzera nyumba yake
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena