Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 June tsamba 3
  • Zimene Ulamuliro wa Yehova Ukuchita

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Ulamuliro wa Yehova Ukuchita
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Akusonkhanitsa Banja Lake
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Mtima Wodikira Umatithandiza Kuti Tipirire
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Makonzedwe Okwaniritsira Cholinga cha Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
    Galamukani!—2022
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 June tsamba 3
Mpando wachifumu wa Yehova

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AEFESO 1-3

Zimene Ulamuliro wa Yehova Ukuchita

1:8-10

Ulamuliro wa Yehova ukugwirizanitsa anthu komanso angelo.

  • Ukukonzekeretsa Akhristu odzozedwa kuti akalamulire kumwamba motsogoleredwa ndi Yesu Khristu

  • Ukukonzekeretsa anthu omwe adzakhale padziko lapansi n’kumalamuliridwa ndi Ufumu wa Mesiya

Kodi ndi zinthu ziti zomwe ndingachite pothandiza kuti tizikhala ogwirizana m’gulu la Yehova?

Alongo awiri a mitundu yosiyana akulalikira limodzi; mnyamata ndi bambo ake akupereka moni kwa m’bale wachikulire ku Nyumba ya Ufumu; mwamuna akumvetsera zimene mkazi wake akunena
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena