Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 83
  • Tifunika Kukhala Odziletsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tifunika Kukhala Odziletsa
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Timafunika Kukhala Odziletsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kulimbana ndi Mphamvu ya Uchimo pa Thupi Lochimwa
    Nsanja ya Olonda—1994
  • Samalirani Mzimu ndi Kukhala ndi Moyo!
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Kukulitsa Chipatso cha Kudziletsa
    Nsanja ya Olonda—1991
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 83

Nyimbo 83

Tifunika Kukhala Odziletsa

Losindikizidwa

(Aroma 7:14-25)

1. Timakonda Yehova kwambiri

Koma ndife anthu ochimwa zedi

Choterotu ndi kofunika

Kuti tikhale odziletsa.

2. Satana ndi matupi ochimwa

Tsiku lililonse amatiyesa.

Koma tikadalira M’lungu

Adzateteza mtima wathu.

3. Tanyamula dzina la Yehova

Choncho tisapezeredwe chifukwa.

Pa chilichonse timachita

Tikhale anthu odziletsa.

(Onaninso 1 Akor. 9:25; Agal. 5:23; 2 Pet. 1:6.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena