Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 25
  • Zinthu Zabwino za Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zinthu Zabwino za Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Munda Wokongola
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
  • N’chifukwa Chiyani Tili ndi Moyo?
    Galamukani!—2009
  • Tamandani Mfumu Yamuyaya!
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Madalitso a Yehova Amatilemeretsa
    Nsanja ya Olonda—2001
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 25

Nyimbo 25

Zinthu Zabwino za Mulungu

(Mlaliki 3:11)

1. M’lungu anapanga

Zinthu m’nthaŵi yake.

Kudya, kumwa, ntchito,

Izitu ndimphatso.

Waika zosatha

Mumitima yathu.

Ndi chiyembekezo

Cha moyo wosatha.

2. Yehova afuna

Kupatsa anthufe

Madalitso zedi

Kuti timkondebe.

Anthu adzakhala

Ndi zinthu zabwino;

Nadzakhala ndi

Ya Kunthaŵi yosatha.

3. Ntchito yaikulu

Yomwe taphunzira

Ndiyolalikira;

Timaisamala.

Ndimphatso ya M’lungu

Idzetsa chimwemwe.

Nkanthu kabwinodi

Komwe tili nako.

4. Tikhale anzeru

Mumasiku onse

Tinene za M’lungu

Tichite zabwino.

Ilitu ndigawo

Lomwe tikusankha,

Tichita zonsezi

Ka’mba ka Yehova.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena