Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 94
  • Mfumu Yosatha, Yeretsani Dzina Lanu!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mfumu Yosatha, Yeretsani Dzina Lanu!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Utumiki Wosangalatsa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tamandani Mfumu Yamuyaya!
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Chifukwa Chake Tiyenera Kudziwa Dzina la Mulungu
    Dzina la Mulungu Limene Lidzakhala Kosatha
  • Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 94

Nyimbo 94

Mfumu Yosatha, Yeretsani Dzina Lanu!

(Ezekieli 38:23)

1. Ya ndinu Mulungu yekha,

Kunthaŵi yosadziŵika.

Mwasonyeza chipiliro,

Mpaka mutadziyeretsa.

Chifuno chanu nchosatha;

Ntchitozo zisonya nzeru;

Ufumu wanu wafika,

Kuipa konse kupita.

2. Mlengi waponseponsedi,

Ndinu wakale kaledi!

Mwawona kuipa konse,

Pansi pa mapazi anu.

Mwatipatsa Mwana wanu;

Adzalamula kosatha.

Adzachotsatu adani;

Izi tizipempherera.

3. Aneneri ananena

Za kupulumutsidwatu.

Zikukwaniritsidwadi,

Tikuchitira umboni.

Dziko lathu silidzatha,

Silidzasinthika konse.

Wonetsani ukuluwo,

Dzetsani ulamuliro.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena