Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 204
  • “Ndine Pano! Munditumize Ine”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ndine Pano! Munditumize Ine”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Ine Ndilipo! Nditumizeni”
    Imbirani Yehova
  • “Ine Ndilipo! Nditumizeni”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 204

Nyimbo 204

“Ndine Pano! Munditumize Ine”

(Yesaya 6:8)

1. Lero anthu alitonza

Dzina labwino la Mlungu.

Ena amyesa wankhanza.

Atinso “palibe Mlungu!”

Ndani adzayeretsadi

Dzina lake la Mulungu?

“Mbuye, ine ndiri pano!

Ndidzaimba za inuyo;

(Korasi)

2. Anthu anyoza za Mlungu;

Alibe mantha za iye.

Ena alambira fano;

Ndi kutama Kaisara.

Adzawachenjeza ndani

Za nkhondo yaikuluyo?

“Mbuye, ine ndiri pano!

Ndidzachenjeza zolimba;

(Korasi)

3. Lero ofatsa alira

Chifukwa cha zoipazi.

Mowona afunafuna

Chowonadi chomasula.

Ndani adzawatonthoza

Akufuna chilungamo?

“Mbuye, ine ndiri pano!

Ndidzaphunzitsa ofatsa;

(KORASI)

Palibenso ulemu wina.

Mbuye, munditumize!”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena