Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 92
  • Lalikirani Molimba Mtima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lalikirani Molimba Mtima
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tsanzirani Yesu mwa Kulalikira Molimba Mtima
    Nsanja ya Olonda—2009
  • ‘Lankhulani Mawu a Mulungu Molimba Mtima’
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Kodi Mumalalikira Molimba Mtima?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2000
  • Pitirizani Kulankhula Mawu a Mulungu Molimbika Mtima
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2005
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 92

Nyimbo 92

Lalikirani Molimba Mtima

(Machitidwe 4:13)

1. Atumiki’nu a Yehova,

Limbani Satana apsinja.

Tipeza chilimbikitsochi,

Mu Mawu a Mulungu ndi m’kumva.

Mawu a Mulungu apatsa

Mphamvu nathandiza kumvera.

Monga atumwi akalewo,

Tikondwere ndi kukhazikika.

2. Pakuti tikhulupilira

Mawu a M’lungu m’mbali zonse,

Sitimawopa konse anthu

Tikhulupilira molimbadi.

Tisamalire ntchito yathu

Ya kulalika m’dziko lonse.

Mwa kulalika molimbika,

Tikhalabe abwenzi a M’lungu.

3. Thandizani ofo’ka onse,

Kuti anene molimbika.

Musasiyetu atsopano;

Athandizeni kuchotsa mantha.

Tonthozani onse olira;

Ndi kudalira pa Mulungu.

Adzalamula m’dziko lonse

Kuti anthu onse amtamande.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena