Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 31
  • Changu Kaamba ka Nyumba ya Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Changu Kaamba ka Nyumba ya Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Achangu Pantchito Zokoma”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kodi Ndinu “Odzipereka pa Ntchito Zabwino”?
    Nsanja ya Olonda—2013
  • “Yakani ndi Mzimu”
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Kodi Mutsanzira Kudzipereka kwa Yehova ndi Yesu pa Nyengo ya Chikumbutso Ikubwerayi?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 31

Nyimbo 31

Changu Kaamba ka Nyumba ya Yehova

(Yohane 2:17)

1. Yesu anali wachangu

Panyumba ya Yehova.

Monga moto womayaka,

Povumbula choipa.

Anadza kupulumutsa,

Nasonyeza cho’nadi.

Ka’mba ka ulemu wa Ya

Anadyedwa ndi changu.

2. Atumwi ndi ophunzira

Analinso achangu.

Mothandizidwa ndi mzimu,

Mipingo inakula!

Sanaleke kulalika,

Namka kunyumba zonse.

Adati chipulumutso,

Nati anthu alape.

3. Lero tikuwona anthu

Achangu m’chilungamo.

Palibe chowabwevutsa

M’dziko loipa lino.

M’lungu awalimbikitsa;

Amtumikira iye.

Alalikabe Ufumu,

Ngachangube, ngolimba.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena