Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 70
  • Khalani Monga Yeremiya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani Monga Yeremiya
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Ndaika Mawu Anga M’kamwa Mwako”
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
  • Khalani Wolimba Mtima Ngati Yeremiya
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Yehova Ndi Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Ndiye Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 70

Nyimbo 70

Khalani Monga Yeremiya

(Yeremiya 1:7, 18)

1. Utumiki wa ’fumu

Uli wosangalatsa.

Pakutumikirako,

M’lungu asamalira.

Baibulo nlowona—

Litichenjeza ife—

Potumikira Mulungu

Tidzavutitsidwanso.

2. Pamene Yeremiya,

Akalitu mnyamata

Anatumikira Ya,

Kodi Ya anatani?

‘Ngakhale akumenye,

Ndi mphamvu zawo zonse,

Sadzakulakatu konse,

Ndiwe nsanja yolimba.’

3. Yeremiya anati

M’lungu ali wowona.

Nkana anavutika,

Anatsiriza ntchito.

Dalirani Mulungu,

Ngati Yeremiyayo.

Lalikirani molimba

Ufumu wa Mulungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena