Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 156
  • “Ndifuna”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ndifuna”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Ndikufuna”
    Imbirani Yehova
  • Kristu Chitsanzo Chathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Ndikufuna”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mpando Waufumu Wakumwamba wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 156

Nyimbo 156

“Ndifuna”

(Luka 5:13)

1. Wona chikondi cha Yesu (chikondicho),

Anasiya m’mwamba malo (abwinodi),

Kukhala ndi anthu, Kupatsa cho’nadi.

Inde, cho’nadi ananena.

Anatonthozadi anthu (kalerodi),

Anachiritsa odwala.

Pantchitoyo anali wowona,

Chotero anati: “Ndifuna.”

2. O Ya anathandizadi (zowonadi)

Potumiza ‘kapoloyo (wanzeruyo)’

Titumika naye, Pomagwira ntchito,

Kupulumutsa ofooka!

Ndithu aŵa angadziŵe (chowonadi)

Ngati tiwakonda zedi.

Ngati amasiye akafunsa,

Kodi mudzanena: “Ndifuna”?

3. Chikondi chitisonkheza (kwambiridi),

Kulalika mopilira (kudzikoli)

Kwa obuulawo Ndi osukidwawo;

Tifike ofuna cho’nadi.

Nchimwemwe pomwe adziŵa (chowonadi)

Cho’nadi cha Baibulo,

Pochita utumiki wa M’lungu!

Chifukwa mwatitu: “Ndifuna.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena