Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 27
  • Musawaope!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Musawaope!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Musawaope!
    Imbirani Yehova
  • Musawaope
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tsatirani Mfumu Yankhondo!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 27

Nyimbo 27

Musawaope!

(Mateyu 10:28)

1. Pitanibe anthu anga,

Ndi mbiri ya Ufumu.

Musawope adani.

Uzani abwinowo

Kuti Mfumu, Yesu Kristu,

Waponyatu m’daniyo,

Satana adzamangidwa,

Mikhole kumasudwa.

(Korasi)

2. Nkana adani anu ndi

Amphamvu ndi ambiri,

Nkana amwetulire,

Kuwanyenga opusa,

Musawope anthu anga;

Limba musakomoke;

Ndidzasunga anthu anga,

Ndi kuwamasulatu.

(Korasi)

3. Sindidzaiŵala inu,

Ndine mphamvu ndi linga.

Nkana mufe pankhondo,

Imfa ndidzagonjetsa.

Musawope anthu anga;

Nkana akuthupseni

Ndidzasunga inu nonse

Monga mwana wadiso.

(KORASI)

Musawope opha thupi.

Moyo sangawononge.

Khala wokhulupirika;

Kufikira mapeto.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena