Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 100
  • Ndife Gulu Lankhondo la Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndife Gulu Lankhondo la Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Ndife Gulu Lankhondo la Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Wonani Khamu la Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pitirizani Kugwira Ntchito, Kukhala Maso ndi Kudikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 100

Nyimbo 100

Ndife Gulu Lankhondo la Yehova

Losindikizidwa

(Yoweli 2:7)

1. Ndife gulu lankhondo

Lolalikira

Ufumu wa Mulungu.

Ukulamulira.

Timapitabe ndithu

Modzipereka.

Ndife osaopa

Olimba mtima.

(KOLASI)

Ndife gulu lankhondo.

Tikulengeza:

“Ufumu wayamba

Kulamulira.”

2. Ndife anthu a M’lungu

Ofunafuna

Anthu ongadi nkhosa

Omwe asochera.

Tifuna kuwapeza,

N’kuwaphunzitsa,

N’kuwalimbikitsa:

“Tizisonkhana.”

(KOLASI)

Ndife gulu lankhondo.

Tikulengeza:

“Ufumu wayamba

Kulamulira.”

3. Gululi n’la Yehova

N’lokonzekera

Kumenya nkhondo ndithu,

Molimbadi mtima.

Koma tikhale tcheru

Kuti tisagwe.

Zinthu zikavuta

Tisafooke.

(KOLASI)

Ndife gulu lankhondo.

Tikulengeza:

“Ufumu wayamba

Kulamulira.”

(Onaninso Afil. 1:7; Aef. 6:11, 14; Filim. 2.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena