Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 21
  • Anthu Achifundo Amakhala Odala

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Anthu Achifundo Amakhala Odala
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Achimwemwe, Ngachifundo!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • ‘Atate Wanu Ndi Wachifundo’
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Timatumikira Mulungu “Wachifundo Chochuluka”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Kodi Tingasonyeze Bwanji Chifundo?
    Nsanja ya Olonda—2007
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 21

Nyimbo 21

Anthu Achifundo Amakhala Odala

Losindikizidwa

(Mateyo 5:7)

1. Achifundo ndi odala

Kwa M’lungu ndi okongola.

Amauza ’nthu abwino

Kuti akhale n’chifundo.

M’lungu popereka dipo

Anasonyeza chifundo.

Chifukwatu amadziwa

Kuti ndife ofooka.

2. Achifundo ndi odala

Adzawakhululukira.

Kuti zikhale zotheka

Dipo linaperekedwa.

Timasonyeza chifundo

Pofalitsa uthengawo:

“Sangalalani chifukwa

Ufumu wake wayamba.”

3. Yehova pa chiweruzo

Adzachitira chifundo

Onse omwe ndi ofatsa

Poti amamutsanzira.

Chotero tiziyesetsa

Chifundo kuchikulitsa.

Monga Mulungu ndi Yesu,

Chifundo tisonyezetu.

(Onaninso Luka 6:36; Aroma 12:8; Yak. 2:13.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena