Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 119
  • Bwerani Mudzatsitsimulidwe!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Bwerani Mudzatsitsimulidwe!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Bwerani Mudzalimbikitsidwe
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kolalikira
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 119

Nyimbo 119

Bwerani Mudzatsitsimulidwe!

Losindikizidwa

(Aheberi 10:24, 25)

1. Tikukhaladi m’dziko losochera,

Anthu sakudziwa M’lungu.

Tikufunikiradi malangizo

Osonyeza njira yathu.

Misonkhano yathu imathandiza

Kukhala n’chiyembekezo,

Imatilimbikitsa n’kutipatsa

Mphamvu yochita zabwino.

Zimene Yehova watilamula

Ife sitidzazisiya.

Pamisonkhano yathu timapeza

Malangizo oyenera.

2. Yehova akudziwa bwino zinthu

Zomwe timafunikira.

Tikamasonkhana timasonyeza

Kuti timamudalira.

Tikamamvera nkhani za abale

Timalimbikitsidwadi.

Timadziwa kuti sitili tokha,

Iwo atithandizadi.

Poyembekezera Paradaiso

Sitisiya kusonkhana.

Tiziphunzira kugwiritsa ntchito

Nzeru yochoka kumwamba.

(Onaninso Sal. 37:18; 140:1; Miy. 18:1; Aef. 5:16; Yak. 3:17.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena