Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 97
  • Pitani Patsogolo, Inu Atumiki a Ufumu!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pitani Patsogolo, Inu Atumiki a Ufumu!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Pitirizani Kulalikira za Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Patsogolo, Inu Aminisitala Aufumu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pitani Patsogolo Mboninu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pitani Patsogolo Mboninu!
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 97

Nyimbo 97

Pitani Patsogolo, Inu Atumiki a Ufumu!

Losindikizidwa

(2 Timoteyo 4:5)

1. Pitani patsogolo ndithu

Polalikira konse.

Muthandize anthu ofatsa

Cho’nadi achikonde.

Ndi mwayidi kutumikira,

Tikonda kulalikira.

Chitirani umboni M’lungu

Ndi dzina lake loyera.

(KOLASI)

Pitirizani kulalikira

padziko lonse.

Pitirizani kukhala

okhulupirikabe.

2. Atumiki enieninu

Pitani patsogolo.

Timatsatira Mbuye wathu.

Tidzalandira mphoto.

Ndi kofunika kuti anthu

Amve uthenga wa M’lungu.

Yehova atipatsa mphamvu

Ndipo sitiopa kanthu!

(KOLASI)

Pitirizani kulalikira

padziko lonse.

Pitirizani kukhala

okhulupirikabe.

3. Tipite patsogolo tonse,

Amuna ndi akazi.

Otsalira ndi nkhosa zina

Tiziyenda m’cho’nadi.

Wathu si utumiki wamba.

Kwa ife n’ngopatulika.

Tiyeni tisonyeze M’lungu

Kuti ndife oyenera.

(KOLASI)

Pitirizani kulalikira

padziko lonse.

Pitirizani kukhala

okhulupirikabe.

(Onaninso Sal. 23:4; Mac. 4:29, 31; 1 Pet. 2:21.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena