Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 19
  • Mulungu Watilonjeza Paradaiso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mulungu Watilonjeza Paradaiso
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Mulungu Watilonjeza Paradaiso
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Lonjezo la Mulungu la Paradaiso
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Tidzaonana M’Paradaiso”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 19

Nyimbo 19

Mulungu Watilonjeza Paradaiso

Losindikizidwa

(Luka 23:43)

1. M’lungu wathu watilonjeza

Paradaiso wam’tsogolo.

Adzachotsa uchimo, imfa,

Zopweteka ndi misozi.

(KOLASI)

Paradaiso adzafika.

Ndipo sitikukayika.

Khristu adzakwaniritsa

Chifuniro cha Mulungu.

2. Cholinga cha Mulungu n’choti

Yesu aukitse anthu.

Monga Yesu analonjeza,

‘Udzakhala m’Paradaiso.’

(KOLASI)

Paradaiso adzafika.

Ndipo sitikukayika.

Khristu adzakwaniritsa

Chifuniro cha Mulungu.

3. Yesu Mfumu, analonjeza

Paradaiso padzikoli.

Tiyamika Atate wathu

Mochokera mumtimamu.

(KOLASI)

Paradaiso adzafika.

Ndipo sitikukayika.

Khristu adzakwaniritsa

Chifuniro cha Mulungu.

(Onaninso Mat. 5:5; 6:10; Yoh. 5:28, 29.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena