Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 15
  • Timadzipereka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Timadzipereka
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Tizilalikira Modzipereka
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 15

Nyimbo 150

Timadzipereka

(Mateyu 9:37, 38)

  1. Yehovatu watipatsa

    zomwe timafunikira.

    Kuti tizisangalala

    pomwe tikum’tumikira.

    (KOLASI)

    Timadzipereka,

    pom’tumikira.

    Ndipo kulikonse tipita,

    mofunitsitsa.

  2. Padzikoli pali ntchito.

    Kosowa tidzapitako.

    Tikatero tisonyeza.

    kuti ena timakonda.

    (KOLASI)

    Timadzipereka,

    pom’tumikira.

    Ndipo kulikonse tipita,

    mofunitsitsa.

  3. Komwe tili kuli ntchito,

    inde, zofunika luso.

    Zinenero taphunzira.

    Ena tikulalikira.

    (KOLASI)

    Timadzipereka,

    pom’tumikira.

    Ndipo kulikonse tipita,

    mofunitsitsa.

(Onaninso Yoh. 4:35; Mac. 2:8; Aroma 10:14.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena