Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 January tsamba 7
  • Yehova Ndi Mulungu Yemwe Amalosera Zoona

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Ndi Mulungu Yemwe Amalosera Zoona
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • 5. Kukwaniritsidwa kwa Ulosi
    Galamukani!—2007
  • Koresi Wamkulu
    Galamukani!—2013
  • Buku la Ulosi
    Buku la Anthu Onse
  • Nthawi Zonse Mawu a Yehova Amakwaniritsidwa
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 January tsamba 7

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YESAYA 43-46

Yehova Ndi Mulungu Yemwe Amalosera Zoona

Losindikizidwa
Tchati chosonyeza kuti panadutsa zaka 200 kuchokera pamene Yesaya analemba ulosi wake mpaka nthawi imene Babulo anawonongedwa
Mfumu Koresi

Kutatsala zaka pafupifupi 200 kuti mzinda wa Babulo uwonongedwe, Yehova ananeneratu mwatsatanetsatane kudzera mwa Yesaya zimene zidzachitike pogonjetsa mzindawo.

44:27–45:2

  • Koresi ndi amene adzagonjetse Babulo

  • Zitseko za mzindawo zidzakhala zotsegula

  • Mtsinje wa Firate, womwe unkateteza mzindawu, ‘udzaumitsidwa’

Asilikali akuwoloka mtsinje wa Firate utaphwera
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena