Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 January tsamba 2
  • “Ufumu Wakumwamba Wayandikira”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ufumu Wakumwamba Wayandikira”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Diso Lanu Limalunjika Pachinthu Chimodzi?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Tizikhala Moyo Wosalira Zambiri Kuti Titumikire Bwino Mulungu
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Khalani ndi Moyo Wolinganizika, Wopepuka
    Nsanja ya Olonda—1989
  • Kodi Mukudziwa?
    Nsanja ya Olonda—2009
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 January tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MATEYU 1-3

“Ufumu Wakumwamba Wayandikira”

3:4

  • Yohane M’batizi

    Zovala za Yohane zinkasonyezeratu kuti ankakhala moyo wosalira zambiri komanso kuti anali wodzipereka pochita chifuniro cha Mulungu

  • Yohane anali ndi mwayi wapadera kwambiri wogwira ntchito yodziwitsa anthu za kubwera kwa Yesu

Kukhala ndi moyo wosalira zambiri kungatithandize kuti tizichita zochuluka potumikira Mulungu ndipo tingamakhale osangalala. Kuti tikhale ndi moyo wosalira zambiri tiyenera . . .

  • kuzindikira zinthu zomwe ndi zofunikadi

  • kusiya kugula zinthu zosafunika kwenikweni

  • kulemba bajeti

  • kuchotsa zinthu zimene sitizigwiritsa ntchito

  • kulipira ngongole zonse

  • kuchepetsa nthawi imene timagwira ntchito

Uchi wam’tchire komanso dzombe

Yohane ankangodya dzombe ndi uchi

Kodi ndingakwaniritse cholinga chiti ngati nditamakhala moyo wosalira zambiri?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena