Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 January tsamba 4
  • Pitirizani Kufunafuna Ufumu Choyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pitirizani Kufunafuna Ufumu Choyamba
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Mmene Muyenera Kulimvera Pemphero la Ambuye
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Yehova Amatipatsa Zimene Timafunikira Tsiku Lililonse
    Nsanja ya Olonda—2004
  • “Tiphunzitseni Ife Kupemphera”
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Kodi Ndizipemphera Bwanji?—Kodi Ndizigwiritsa Ntchito Pemphero la Ambuye?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 January tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MATEYU 6-7

Pitirizani Kufunafuna Ufumu Choyamba

M’pemphero lachitsanzo, Yesu anasonyeza kuti zinthu zokhudza kukwaniritsidwa kwa cholinga cha Yehova komanso Ufumu wa Mulungu ndi zimene ziyenera kukhala zofunika kwambiri pamoyo wathu.

6:9-13

  • Yesu ali kumwamba pampando wake wachifumu

    Dzina la Mulungu

    Ufumu wa Mulungu

    Chifuniro cha Mulungu

  • Mkate

    Chakudya cha tsiku ndi tsiku

    Kukhululukidwa machimo

    Kupulumutsidwa pa mayesero

Zinthu zina zokhudza Ufumu zimene ndiyenera kupempherera:

  • Ntchito yolalikira ipite patsogolo

  • Mzimu woyera uthandize anthu amene akuzunzidwa

  • Mulungu adalitse ntchito yomanga kapena ntchito yolalikira imene yakonzedwa mwapadera

  • Mulungu azipereka nzeru komanso mphamvu kwa anthu amene akutsogolera m’gulu lake

  • Zina

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena