Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 February tsamba 6
  • Kodi Mumayendera Maganizo a Ndani?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mumayendera Maganizo a Ndani?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Nyamula Mtengo Wako Wozunzikirapo, ndi Kunditsatira Mosalekeza
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Tisakhalenso ndi Moyo mwa Ife Tokha
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Kutumikira Yehova ndi Mzimu Wodzimana
    Nsanja ya Olonda—1993
  • Anakhalabe Wokhulupirika pa Nthawi Yovuta
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 February tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MATEYU 16-17

Kodi Mumayendera Maganizo a Ndani?

16:21-23

Yesu akuuza Petulo kuti apite kumbuyo kwake
  • N’kutheka kuti Petulo anauza Yesu kuti adzikomere mtima ndi cholinga chabwino koma mwansanga Yesu anawongolera maganizo olakwika amene Petulo anali nawo

  • Yesu ankadziwa kuti imeneyo sinali nthawi yoti ‘adzikomere mtima.’ Akanachita zimenezi akanakhala akuchita zimene Satana ankafuna

16:24

Yesu anatchula zinthu zitatu zotsatirazi zomwe tiyenera kuchita ngati tikufuna kuti Mulungu azititsogolera. Kodi zinthu zimenezi zikutanthauza chiyani?

  • Kudzikana:

  • Kunyamula mtengo wozunzikirapo:

  • Kutsatira Yesu mosalekeza:

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena