Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 November tsamba 6
  • Mpingo Watsopano Wachikhristu Unayesedwa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mpingo Watsopano Wachikhristu Unayesedwa
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Yendani M’kuwopa kwa Yehova
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • “Sitefano Anali ndi Mphamvu Ndipo Ankachita Kuonekeratu Kuti Mulungu Ali Naye”
    ‘Kuchitira Umboni Mokwanira za Ufumu wa Mulungu’
  • Kodi Yehova Amafuna Kuti Tizichita Chiyani?
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Stefano Aponyedwa Miyala
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 November tsamba 6
Saulo akuonerera pamene Sitefano akuphedwa poponyedwa miyala

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 6-8

Mpingo Watsopano Wachikhristu Unayesedwa

6:1-7; 7:58–8:1

Akazi amasiye olankhula Chigiriki omwe anali atangobatizidwa kumene, amene anakhalabe kwa kanthawi ku Yerusalemu, ankasalidwa. Kodi iwo anakhumudwa ndi zimenezi, kapena anadikira moleza mtima kuti Yehova athetse nkhaniyo?

Sitefano ataponyedwa miyala, komanso anthu atayamba kuzunza Akhristu a mumpingo wa ku Yerusalemu, ambiri anathawira ku Yudeya ndi ku Samariya. Koma kodi zimenezi zinachititsa kuti abwerere m’mbuyo pankhani yolalikira?

Ngakhale kuti mpingo wachikhristu unakumana ndi mavuto amenewa, unapitirizabe kukula chifukwa chakuti Yehova ankauthandiza.​—Mac. 6:7; 8:4.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ineyo ndimatani ndikakumana ndi mayesero?’

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena