Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 74
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • Gwirizanani Nawo m’Nyimbo Yaufumu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • M’patseni Yehova Ulemerero
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 74

NYIMBO 74

Tiimbire Limodzi Nyimbo ya Ufumu

Losindikizidwa

(Salimo 98:1)

  1. 1. Iyi ndi nyimbo yachisangalalo

    Yolemekeza M’lungu wamkulu.

    Imatipatsadi chiyembekezo.

    Imbani nafe nyimbo yathuyi.

    (KOLASI)

    Lambirani M’lungu wathu.

    Mwana wake ndiye Mfumu.

    Dzaphunzireni nyimbo ya Ufumu.

    Tamandani dzina la Mulungu.

  2. 2. Nyimboyi ikulengeza Ufumu.

    Yesu Khristu ndi wolamulira

    Ndipo mtundu watsopano wabadwa,

    Nawo ukumusangalalira.

    (KOLASI)

    Lambirani M’lungu wathu.

    Mwana wake ndiye Mfumu.

    Dzaphunzireni nyimbo ya Ufumu.

    Tamandani dzina la Mulungu.

  3. 3. Amene angaphunzire nyimboyi

    Ndi amene amadzichepetsa.

    Ambiri m’dzikoli aiphunzira

    Ndipo akuphunzitsanso ena.

    (KOLASI)

    Lambirani M’lungu wathu.

    Mwana wake ndiye Mfumu.

    Dzaphunzireni nyimbo ya Ufumu.

    Tamandani dzina la Mulungu.

(Onaninso Sal. 95:6; 1 Pet. 2:​9, 10; Chiv. 12:10.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena