Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 73
  • Tithandizeni Kukhala Olimba Mtima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tithandizeni Kukhala Olimba Mtima
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tithandizeni Kukhala Olimba Mtima
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • ‘Lankhulani Mawu a Mulungu Molimba Mtima’
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Tsanzirani Yesu mwa Kulalikira Molimba Mtima
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Kodi Mumalalikira Molimba Mtima?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2000
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 73

NYIMBO 73

Tithandizeni Kukhala Olimba Mtima

Losindikizidwa

(Machitidwe 4:29)

  1. 1. Polalikira Ufumu

    Komanso dzina lanu,

    Anthu ena amatsutsa

    Ndiponso kutinyoza.

    Koma sitiwaopa

    Timamvera inu nokha.

    Choncho Yehova tikupempha

    Mutipatse mzimu wanu.

    (KOLASI)

    Polalikira uthenga

    Mutichotsere mantha.

    Tikhale olimba mtima,

    Anthu amve uthenga.

    Amagedo ikufika,

    Tikhale olimba mtima.

    Tithandizeni Yehova,

    Tikupempha.

  2. 2. Pomwe tikuchita mantha

    M’madziwa ndife fumbi.

    Mudzatithandiza ndithu

    Paja munalonjeza.

    Imvani kuopseza

    Kwa anthu odana nafe.

    Tithandizeni tisaope.

    Tikhale olimba mtima.

    (KOLASI)

    Polalikira uthenga

    Mutichotsere mantha.

    Tikhale olimba mtima,

    Anthu amve uthenga.

    Amagedo ikufika,

    Tikhale olimba mtima.

    Tithandizeni Yehova,

    Tikupempha.

(Onaninso 1 Ates. 2:2; Aheb. 10:35.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena