Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 88
  • Ndiphunzitseni Njira Zanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndiphunzitseni Njira Zanu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Ndidziwitseni Njira Zanu
    Imbirani Yehova
  • Muzikonda Kwambiri Choonadi Panokha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi
    Imbirani Yehova
  • Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 88

NYIMBO 88

Ndiphunzitseni Njira Zanu

Losindikizidwa

(Salimo 25:4)

  1. 1. Yehova tasonkhanatu pamodzi

    Pomvera kuitana kwanu.

    Mawu anu ndi nyale m’njira yathu,

    Amatiphunzitsa za inu.

    (KOLASI)

    Ndiphunzitseni njira zanuzo,

    Ndikhale womvera malamulo.

    Ndiyendetseni m’njira yoona,

    Ndizikonda malamulo anu.

  2. 2. Nzeru zanu Yehova ndi zozama.

    Mfundo zanu n’zolimbikitsa.

    Mawu anu adzakhala kosatha,

    Timapezamo zodabwitsa.

    (KOLASI)

    Ndiphunzitseni njira zanuzo,

    Ndikhale womvera malamulo.

    Ndiyendetseni m’njira yoona,

    Ndizikonda malamulo anu.

(Onaninso Eks. 33:13; Sal. 1:2; 119:​27, 35, 73, 105.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena