Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • ed tsamba 31
  • Mawu Omaliza

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Omaliza
  • Mboni za Yehova ndi Maphunziro
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi a Mboni za Yehova Ndi Akhristu Enieni?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Mboni za Yehova
    Kukambitsirana za m’Malemba
  • Kodi Ana Ayenera Kuphunzitsidwa za Mulungu?
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Kodi a Mboni za Yehova Amakakamiza Ana Awo Kuti Akhalenso a Mboni?
    Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
Onani Zambiri
Mboni za Yehova ndi Maphunziro
ed tsamba 31

Mawu Omaliza

SITIKHOZA kufotokoza zonse ponena za zikhulupiriro za chipembedzo za Mboni za Yehova m’brosha lino. M’malo mwake, tangolongosola zikhulupiriro zina za Mboni ndi kusonyeza bwino lomwe mkhalidwe wa banja umene ukuyambukira mwana wanu wa sukulu ngati kholo limodzi kapena onse aŵiri ali Mboni.

Mboni za Yehova zimaika chisamaliro chachikulu pa kakulidwe kauzimu ka ana awo. Ndipo zili ndi chidaliro chakuti zimenezi zimachirikiza kukula kwa ana awo m’zinthu zina. Zikhulupiriro zawo ndi malamulo omwe zimatsatira zimachititsa moyo wawo kukhala ndi chifuno ndi kuwathandiza kuchita ndi mavuto a tsiku ndi tsiku. Ndiponso, zikhulupiriro ndi malamulo amenewo zimawasonkhezera kukhala ana a sukulu akhama ndi nzika zabwino kwa moyo wawo wonse.

Mboni zimaona moyo moona mtima, chotero zimaika chisamaliro chachikulu pa maphunziro. Chifukwa chake, zimafuna kugwira ntchito limodzi nanu malinga ndi kukhoza kwawo. Komabe izo zidzapitirizabe kulimbikitsa ana awo, m’nyumba zawo ndi pamalo awo olambirira, kotero kuti zichite mbali yawo m’ntchito yogwirizana ndi yopindulitsa imeneyi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena