Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yp2 tsamba 4-5
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
  • Timitu
  • CHIGAWO 1
  • CHIGAWO 2
  • CHIGAWO 3
  • CHIGAWO 4
  • CHIGAWO 5
  • CHIGAWO 6
  • CHIGAWO 7
  • CHIGAWO 8
  • CHIGAWO 9
Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
yp2 tsamba 4-5

Zamkatimu

6 Mawu Oyamba: Kodi Malangizo Abwino Ndingawapeze Kuti?

CHIGAWO 1

KUSIRIRA MNYAMATA KAPENA MTSIKANA

14 1 Kodi Ndafika Poti N’kukhala ndi Chibwenzi?

21 2 Kodi Kuchita Chibwenzi Mobisa N’koopsa Motani?

28 3 Kodi Munthu Ameneyu Ndi Woyenera Kuti Ndimange Naye Banja?

42 4 Kodi Tiyenera Kusonyezana Chikondi Mpaka Pati?

48 5 N’chifukwa Chiyani Sindiyenera Kugonana ndi Aliyense Mpaka N’talowa M’banja?

CHIGAWO 2

KUSINTHA KWA THUPI

58 6 Kodi Thupi Langali Latani?

67 7 Kodi Ndingatani Ngati Sindikusangalala ndi Mmene Ndikuonekera?

74 8 Kodi Ndinalakwa Chiyani Kuti Ndidwale Chonchi?

CHIGAWO 3

ANZANU

86 9 Kodi Ndingatani Ngati Ndikusowa Ocheza Nawo?

92 10 N’chifukwa Chiyani Mnzanga Wayamba Kudana Nane?

99 11 Kodi ndi Bwino Kucheza pa Intaneti?

105 12 Kodi Miseche ndi Yoipa Bwanji?

CHIGAWO 4

MOYO WA KUSUKULU

114 13 Kodi Ndingatani Kuti Ndizikhoza Bwino Kusukulu?

121 14 Kodi Ndingatani Anzanga Akamandivutitsa Kusukulu?

128 15 Kodi Ndingapewe Bwanji Kutengera Zochita za Anzanga?

136 16 N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kuulula Zimene Ndimachita Mseri?

142 17 Kodi ndi Bwino Kucheza ndi Anzanga a Kusukulu?

CHIGAWO 5

NKHANI ZOKHUDZA NDALAMA

150 18 Kodi Ndingatani Kuti Ndizipeza Ndalama?

156 19 Kodi Ndingatani Kuti Ndizigwiritsa Ntchito Ndalama Mwanzeru?

165 20 Kodi Ndingachite Chiyani Ngati Banja Lathu ndi Losauka?

CHIGAWO 6

MAKOLO ANU

174 21 Kodi Ndingatani Ngati Makolo Anga Amandidzudzula Pachilichonse?

181 22 N’chifukwa Chiyani Makolo Anga Anandiikira Malamulo Ambirimbiri?

190 23 Ndingatani Makolo Anga Akamaledzera Kapena Kumwa Mankhwala Osokoneza Bongo?

199 24 Kodi Ndingatani Makolo Anga Akamakangana?

208 25 Kodi Ndingasangalale Ngakhale Kuti Ndikuleredwa ndi Bambo Kapena Mayi Okha?

CHIGAWO 7

MTIMA WANU

218 26 Kodi Ndingatani Kuti Ndisamakonde Kupsa Mtima Ndiponso Kukhumudwa?

225 27 N’chifukwa Chiyani Sindifuna Kulakwitsa Chilichonse?

231 28 Kodi Ndingapewe Bwanji Mtima Wofuna Kugonana ndi Amuna Kapena Akazi Anzanga?

237 29 Kodi Ndingatani Kuti Ndisamangoganiza za Anyamata Kapena Atsikana?

CHIGAWO 8

ZOSANGALATSA

246 30 Kodi Ndiyenera Kuchita Masewera a Pakompyuta?

253 31 Kodi Ndingatani Kuti Ndisamangokhalira Kumvetsera Nyimbo?

263 32 Kodi Ndizichita Zosangalatsa Zotani?

273 33 N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kupewa Kuona Zithunzi Zolaula?

CHIGAWO 9

KUKULA MWAUZIMU

282 34 N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kutsatira Mfundo za M’Baibulo?

289 35 Kodi Ndingatani Kuti Ndikhale Paubwenzi ndi Mulungu?

297 36 Kodi Ndingafotokoze Motani Zimene Ndimakhulupirira Zokhudza Mulungu?

304 37 Kodi Ndiyenera Kubatizidwa?

311 38 Kodi Ndidzachite Zotani Pamoyo Wanga?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena