Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 39
  • Mtendere Wathu Wamtengo Wapatali

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mtendere Wathu Wamtengo Wapatali
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Amatipatsa Mtendere
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukhala Kwathu ndi Mtendere
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Lolani “Mtendere wa Mulungu” Uchinjirize Mtima Wanu
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Mtendere Weniweni—Kodi Udzachokera Kuti?
    Nsanja ya Olonda—1997
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 39

Nyimbo 39

Mtendere Wathu Wamtengo Wapatali

Losindikizidwa

(Yohane 14:27)

1. Tamandani Yehova

Wamtendereyo.

Nkhondo adzazithetsa

Mwa Mwana wake,

Ndipo adzapambana

Nkhondo yabwino

N’kubweretsa mtendere

Padziko lonse.

2. Ukali ndi mkangano,

Izi tasiya.

Mikondo ndi lupanga

Zonse tataya.

Tilitu pa mtendere

Ndi anthu onse.

Monga nkhosa za Yesu,

Ee, zamtendere.

3. Mtendere ndi chipatso

Chachilungamo,

Ndi nzeru yakumwamba,

Yomwe tipempha.

Tiyendebe m’njirayi,

Timaikonda,

Mtendere udzakhala

Padziko lonse.

(Onaninso Sal. 46:9; Yes. 2:4; Yak. 1:17, 18.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena