Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/13 tsamba 3
  • Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 10/13 tsamba 3

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu

Mafunso otsatirawa tidzawakambirana pa Sukulu ya Utumiki wa Mulungu ya mlungu woyambira October 28, 2013.

1. Kodi kukhala ndi “maganizo a Khristu” kumatanthauza chiyani? (1 Akor. 2:16) [Sept. 2, w08 7/15 tsa. 27 ndime 7]

2. Kodi tingasonyeze bwanji kuti ‘timathawa dama’? (1 Akor. 6:18) [Sept. 2, w08 7/15 tsa. 27 ndime 9; w04 2/15 tsa. 12 ndime 9]

3. Kodi Paulo ankatanthauza chiyani pamene ananena kuti, “akazi akhale chete m’mipingo”? (1 Akor. 14:34) [Sept. 9, w12 9/1 tsa. 9, bokosi]

4. Kodi mawu a Paulo amene ali pa 2 Akorinto 1:24 angathandize bwanji akulu masiku ano? [Sept. 16, w13 1/15 tsa. 27 ndime 2-3]

5. Kodi tingatsatire bwanji zimene lemba la 2 Akorinto 9:7 limanena? [Sept. 23, g 5/08 tsa. 21, bokosi]

6. Kodi kutsatira malangizo a Paulo a pa Agalatiya 6:4, kungatithandize bwanji? [Sept. 30, w12 12/15 tsa. 13 ndime 18]

7. Kodi “kusunga umodzi wathu mwa mzimu” kumatanthauza chiyani? (Aef. 4:3) [Oct. 7, w12 7/15 tsa. 28 ndime 7]

8. Kodi Paulo ankaona bwanji zinthu zimene anazisiya? (Afil. 3:8) [Oct. 14, w12 3/15 tsa. 27 ndime 12]

9. Kodi tikuphunzira chiyani pa malangizo akuti: “Tisapitirize kugona ngati mmene enawo akuchitira”? (1 Ates. 5:6) [Oct. 21, w12 3/15 tsa. 10 ndime 4]

10. Kodi imfa ya Yesu inali “dipo lokwanira ndendende” motani? (1 Tim. 2:6) [Oct. 28, w11 6/15 tsa. 13 ndime 11]

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena