LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 3/15 tsa. 8
  • Maulaliki Acitsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maulaliki Acitsanzo
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Zofanana
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
Onaninso Zina
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 3/15 tsa. 8

Maulaliki Acitsanzo

NSANJA YA MLONDA March-April

Tikugaŵila kapepala ka uthenga aka kwa aliyense. [Patsani mwininyumba kapepala kakuti Kodi Baibo Mumaiona Bwanji? ndi kum’funsa mafunso ali patsambo loyamba. Musonyezeni yankho la m’Baibulo pa 2 Timoteyo 3:16 ndi kumulimbikitsa kuti apeze nthawi yoŵelenga kapepalako.] Ena amakaikila ngati Baibulo lili ndi malangizo amene angawathandize pankhani ya nchito yao? Onani zimene Baibulo limanena pankhani ya nchito. [Ŵelengani Mlaliki 3:13.] Magazini iyi ikufotokoza mfundo za m’Baibulo zimene zingatithandize kuti tizisangalala ndi nchito. Kodi ndingakusiileni magaziniyi?

Galamukani! April

Lelo tikuceza ndi mabanja mwacidule. Anthu ambili amada nkhawa ndi kusintha kumene amaona m’mabanja. Kale ana anali kumvela makolo koma tsopano m’mabanja ena, ana samvela makolo. Kodi muganiza kuti makolo asiya kulangiza ana ao? [Yembekezani yankho.] Malinga ndi zimene Baibulo limanena cilango n’cofunika kwambili. [Ŵelengani Miyambo 29:17.] Magazini ino ifotokoza malangizo othandiza pa kupeleka cilango kwa ana.”

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani