LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 September tsa. 3
  • Yesu Alalikila Mayi Wacisamariya

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yesu Alalikila Mayi Wacisamariya
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • 4:6-26, 39-41
  • Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuyambitsa Makambilano ndi Colinga Cakuti Ticite Ulaliki Wamwai
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Mzimayi Akumana na Yesu pa Citsime
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Yesu Ali Pacitsime Ndi Mkazi
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuyambitsa Makambilano Otsogolela ku Ulaliki
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 September tsa. 3
Yesu akamba na mzimayi wacisamariya pa citsime; mzimayi wacisamariya auza ena za Yesu

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YOHANE 3-4

Yesu Alalikila Mayi Wacisamariya

4:6-26, 39-41

N’ciani cinathandiza Yesu kucita ulaliki wamwayi?

  • 4:7—Iye anayambitsa makambilano mwa kupempha madzi akumwa m’malo mokamba za Ufumu, kapena kudziulula kuti ni Mesiya

  • 4:9—Iye sanaweluziletu mayi wacisamariya cifukwa ca mtundu wake

  • 4:9, 12—Pamene mayiyo anayambitsa nkhani zofuna kubweletsa mkangano, Yesu sanapatuke pa mfundo imene anali kuifotokoza.—cf peji 77 pala. 3

  • 4:10—Iye anayambitsa makambilano ake mwa kuseŵenzetsa cinthu codziŵika kwa mayiyo

  • 4:16-19—Yesu anakamba na mayiyo mwaulemu olo kuti anali kukhala umoyo waciwelewele

Kodi nkhaniyi ionetsa bwanji kufunika kocita ulaliki wamwayi?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani