LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 May tsa. 10
  • Kusonkhana Pamodzi Kumatipindulila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kusonkhana Pamodzi Kumatipindulila
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Analigaŵa Mwanzelu Dziko la Kanani
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Tetezani Coloŵa Canu Camtengo Wapatali
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Yehova Amapatula Anthu Ake
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Muzilimbikitsa Ena pa Nthawi Zovuta
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 May tsa. 10

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kusonkhana Pamodzi Kumatipindulila

Hezekiya anakonza phwando lalikulu pa Pasika ku Yerusalemu (2 Mbiri 30:1;it-1 1103 ¶2)

Anthu ambili anapezekapo ngakhale kuti panali otsutsa (2 Mbiri 30:10, 11, 13; it-1 1103 ¶3)

Iwo anasangalala kwambili ndipo analimbikitsidwa kutumikila Yehova (2 Mbiri 25–31:1; it-1 1103 ¶4-5)

Alongo aŵili akumbatilana mwacimwemwe pa Nyumba ya Ufumu. Onse opezeka pa msonkhanowo avala mamasiki.

DZIFUNSENI KUTI: ‘Kodi napindula bwanji cifukwa copezeka pa misonkhano yampingo komanso ikuluikulu ya pamaso-m’pamaso?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani